Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yesaya 52:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Panali anthu ambiri amene ankamuyangʼana modabwa,

      Chifukwa maonekedwe ake anali atasintha kwambiri kuposa a munthu wina aliyense,

      Ndipo kukongola kwa thupi lake kunali kutatha, sanalinso wokongola kuposa anthu,

  • Yohane 1:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Iye anali mʼdziko+ ndipo dziko linakhalapo kudzera mwa iye,+ koma dzikolo silinamudziwe.

  • Afilipi 2:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Ayi sanachite zimenezo, koma anasiya zonse zimene anali nazo nʼkukhala ngati kapolo+ ndipo anakhala munthu.*+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena