Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Mateyu 27:12-14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Koma pamene ansembe aakulu komanso akulu ankamuneneza, iye sanayankhe chilichonse.+ 13 Ndiyeno Pilato anamufunsa kuti: “Kodi sukumva zinthu zambirimbiri zimene akukunenezazi?” 14 Koma iye anangokhala chete, osamuyankha chilichonse, moti bwanamkubwayo anadabwa kwambiri.

  • Machitidwe 8:32, 33
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 32 Mawu a mʼMalemba amene ankawerengawo anali akuti: “Anamutengera kumalo oti akamuphere ngati nkhosa. Ndipo mofanana ndi mwana wa nkhosa amene wangokhala chete pamene akufuna kumumeta ubweya, sanatsegule pakamwa pake.+ 33 Pamene ankamuchititsa manyazi, sanamuchitire zachilungamo.+ Ndi ndani angafotokoze mwatsatanetsatane mʼbadwo wa makolo ake? Chifukwa moyo wake wachotsedwa padziko lapansi.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena