Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Maliko 15:27
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 27 Komanso iwo anapachika pamtengo achifwamba awiri limodzi ndi iye. Mmodzi anamupachika kudzanja lake lamanja ndipo wina anali kumanzere kwake.+

  • Luka 22:37
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 37 Chifukwa ndikukuuzani kuti zimene zinalembedwa ziyenera kukwaniritsidwa mwa ine, zakuti, ‘Iye anaikidwa mʼgulu la anthu osamvera malamulo.’+ Zili choncho chifukwa zimene zinanenedwa zokhudza ine zikukwaniritsidwa.”+

  • Luka 23:32, 33
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 32 Anthuwo anatenganso amuna ena awiri, amene anali zigawenga, kuti akawaphe limodzi ndi Yesu.+ 33 Ndiyeno atafika pamalo otchedwa Chibade,+ anamukhomerera pamtengo limodzi ndi zigawenga zija. Mmodzi anamupachika kudzanja lake lamanja ndipo wina anali kumanzere kwake.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena