Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yesaya 49:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 Yehova wanena kuti:

      “Pa nthawi yosonyeza kukoma mtima kwanga, ndinakuyankha.+

      Ndipo pa tsiku la chipulumutso ndinakuthandiza.+

      Ndinkakuteteza kuti ndikupereke ngati pangano kwa anthu,+

      Kuti ndikonzenso dzikolo,

      Kuti anthuwo atengenso cholowa chawo chimene chinali bwinja,+

  • Ezekieli 36:35
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 35 Anthu adzanena kuti: “Dziko limene linali bwinja tsopano lakhala ngati munda wa Edeni.+ Mizinda imene inawonongedwa ija, imene inali mabwinja ndiponso imene nyumba zake zinagwetsedwa, tsopano ili ndi mipanda yolimba kwambiri ndipo mukukhala anthu.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena