Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yesaya 44:26
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 26 Ndine amene ndimachititsa mawu a mtumiki wanga kuti akwaniritsidwe

      Ndiponso amene ndimakwaniritsa mawu onse amene amithenga anga analosera.+

      Ndine amene ndikunena za Yerusalemu kuti, ‘Muzidzakhala anthu.’+

      Ndikunenanso za mizinda ya ku Yuda kuti, ‘Idzamangidwanso,+

      Ndipo ndidzakonza malo ake amene anawonongedwa.’+

  • Yesaya 58:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Chifukwa cha inu, anthu adzamanganso mabwinja akalekale,+

      Ndipo mudzabwezeretsa maziko a mibadwo yakale.+

      Mudzatchedwa womanga makoma ogumuka,+

      Ndiponso wokonza misewu kuti anthu azikhala mʼmphepete mwake.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena