-
Yesaya 44:26Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
26 Ndine amene ndimachititsa mawu a mtumiki wanga kuti akwaniritsidwe
Ndiponso amene ndimakwaniritsa mawu onse amene amithenga anga analosera.+
Ndine amene ndikunena za Yerusalemu kuti, ‘Muzidzakhala anthu.’+
Ndikunenanso za mizinda ya ku Yuda kuti, ‘Idzamangidwanso,+
Ndipo ndidzakonza malo ake amene anawonongedwa.’+
-