Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yesaya 42:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 42 Taonani mtumiki wanga+ amene ndikumuthandiza,

      Wosankhidwa wanga+ amene amandisangalatsa,+

      Ine ndaika mzimu wanga mwa iye.+

      Iye adzabweretsa chilungamo kwa anthu a mitundu ina.+

  • Mateyu 12:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 “Taonani mtumiki wanga+ amene ndamusankha, wokondedwa wanga, amene amandisangalatsa kwambiri.+ Ndidzaika mzimu wanga pa iye+ ndipo anthu a mitundu ina adzawasonyeza bwinobwino chilungamo chenicheni.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena