Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Mbiri 32:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Ndiyeno Yehova anatumiza mngelo yemwe anapha msilikali aliyense wamphamvu,+ mtsogoleri ndiponso mkulu wa asilikali aliyense mumsasa wa mfumu ya Asuri, moti mfumuyo inabwerera kwawo mwamanyazi. Kenako inalowa mʼkachisi wa mulungu wake ndipo ena mwa ana ake anaipha ndi lupanga mʼkachisimo.+

  • Yesaya 30:32
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 32 Ulendo uliwonse umene Yehova adzakwapule Asuri

      Ndi ndodo yake yoperekera chilango,

      Kudzamveka kulira kwa maseche ndi azeze+

      Pamene akukweza dzanja lake kuti awalange pankhondo.+

  • Nahumu 3:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 Aliyense wokuona adzakuthawa+ ndipo adzanena kuti,

      ‘Nineve wawonongedwa!

      Ndani adzamumvere chisoni?’

      Kodi anthu oti akutonthoze ndidzawapeza kuti?

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena