Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Mika 3:2-4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Koma mumadana ndi zinthu zabwino+ ndipo mumakonda zinthu zoipa.+

      Mumasenda khungu la anthu anga nʼkuchotsa mnofu pamafupa awo.+

       3 Mumadyanso mnofu wa anthu anga,+

      Ndipo mumasenda khungu lawo.

      Mumaswa mafupa awo nʼkuwaphwanyaphwanya.+

      Ngati zinthu zimene zaphikidwa mumphika* komanso ngati nyama imene ili mumphika.

       4 Pa nthawiyo adzafuulira Yehova kuti awathandize,

      Koma sadzawayankha.

      Adzawabisira nkhope yake pa nthawi imeneyo,+

      Chifukwa cha zochita zawo zoipa.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena