Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yeremiya 46:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 “Lengezani zimenezi mu Iguputo, muzilengeze ku Migidoli.+

      Lengezani zimenezi ku Nofi* ndi ku Tahapanesi.+

      Munene kuti, ‘Imani mʼmalo anu ndipo mukhale okonzeka,

      Chifukwa lupanga lidzawononga anthu onse amene akuzungulirani.

  • Ezekieli 30:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Yehova, Ambuye Wamkulu Koposa, wanena kuti: ‘Ndidzawononganso mafano onyansa* nʼkuthetsa milungu yopanda pake ya ku Nofi.*+ Sipadzapezekanso kalonga* wochokera mʼdziko la Iguputo ndipo ndidzachititsa kuti anthu amʼdzikolo azikhala mwamantha.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena