Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yesaya 11:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Padzakhala msewu waukulu+ wochokera kudziko la Asuri woti mudzadutse anthu ake amene adzatsale,+

      Ngati mmene zinalili kwa Aisiraeli pamene ankatuluka mʼdziko la Iguputo.

  • Yesaya 35:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 Kumeneko kudzakhala msewu waukulu+

      Inde msewu umene udzatchedwe Msewu Wopatulika.

      Munthu wodetsedwa sadzayenda mumsewu umenewo.+

      Amene adzayendemo ndi munthu yekhayo amene ali woyenerera.

      Palibe munthu wopusa amene adzayende mumsewu umenewo.

  • Yesaya 40:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  3 Winawake akufuula mʼchipululu kuti:

      “Konzani njira ya Yehova!+

      Mulungu wathu mukonzereni msewu wowongoka+ wodutsa mʼchipululu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena