Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yeremiya 51:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 “Nolani mivi yanu.*+ Tengani zishango zozungulira.

      Yehova walimbikitsa* mafumu a Amedi kuti akamenye nkhondo,+

      Chifukwa akufuna kuwononga Babulo.

      Yehova akubwezera Babulo, akumubwezera chifukwa cha kachisi wake.

  • Yeremiya 51:28
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 28 Sankhani* mitundu ya anthu kuti ichite naye nkhondo.

      Sankhani mafumu a ku Mediya,+ abwanamkubwa ake ndi achiwiri kwa olamulira awo onse

      Komanso mayiko onse amene iwo amawalamulira.

  • Danieli 5:28
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 28 PERESI, ufumu wanu wagawidwa ndipo waperekedwa kwa Amedi ndi Aperisiya.”+

  • Danieli 5:30
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 30 Usiku womwewo, Belisazara mfumu ya Akasidi anaphedwa.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena