Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 137:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 137 Tinakhala pansi mʼmphepete mwa mitsinje ya ku Babulo.+

      Tinalira titakumbukira Ziyoni.+

  • Yesaya 14:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 mudzanena mwambi uwu wonyoza mfumu ya Babulo:

      “Amene ankagwiritsa ntchito anzake mokakamiza uja wawonongedwa!

      Kuponderezedwa kuja kwatha ndithu!+

  • Yesaya 14:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 Tsopano dziko lonse lapansi lapuma, palibenso chosokoneza.

      Anthu akufuula mosangalala.+

  • Yesaya 35:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Anthu amene Yehova anawawombola adzabwerera+ ndipo adzafika ku Ziyoni akufuula mosangalala.+

      Chisangalalo chosatha chidzakhala ngati chisoti chachifumu kumutu kwawo.+

      Adzakhala okondwa ndi osangalala

      Ndipo chisoni ndi kubuula zidzachoka.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena