Yobu 6:19 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 19 Magulu a anthu amalonda a ku Tema+ amaifunafuna,Anthu apaulendo a ku Sheba*+ amaidikirira. Yeremiya 25:17 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 17 Choncho ndinatenga kapu imene inali mʼdzanja la Yehova ndipo ndinamwetsa mitundu yonse imene Yehova ananditumizako. Mitunduyo ndi iyi:+ Yeremiya 25:23 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 23 Ndinamwetsanso Dedani,+ Tema, Buza, onse odulira ndevu zawo zamʼmbali,+
17 Choncho ndinatenga kapu imene inali mʼdzanja la Yehova ndipo ndinamwetsa mitundu yonse imene Yehova ananditumizako. Mitunduyo ndi iyi:+