Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 18:34
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 34 Iye amaphunzitsa manja anga kumenya nkhondo,

      Manja anga angathe kukunga uta wakopa.*

  • Salimo 68:35
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 35 Mulungu walamula kuti anthu amuope komanso amupatse ulemu mʼmalo ake opatulika aulemerero.+

      Iye ndi Mulungu wa Isiraeli,

      Amene amapereka mphamvu ndi nyonga kwa anthu.+

      Mulungu atamandike.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena