Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Mafumu 16:10, 11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Kenako Mfumu Ahazi anapita kukakumana ndi Tigilati-pilesere mfumu ya Asuri ku Damasiko. Kumeneko anaonako guwa lansembe, choncho Mfumu Ahazi anatumizira wansembe Uliya pulani ya guwalo.+ 11 Wansembe Uliya+ anamanga guwalo+ mogwirizana ndi malangizo onse amene Mfumu Ahazi anamutumizira ali ku Damasiko. Wansembe Uliya anamaliza kumanga guwalo Mfumu Ahazi asanabwere kuchokera ku Damasiko.

  • Yeremiya 5:31
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 31 Aneneri akulosera zabodza,+

      Ndipo ansembe akugwiritsa ntchito mphamvu zawo kuti azilamulira ena.

      Anthu anga nawonso akukonda zimenezi.+

      Koma kodi mudzachita chiyani mapeto akadzafika?”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena