Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Maliro 2:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Iwo ankafunsa amayi awo kuti: “Kodi chakudya ndi vinyo zili kuti?”+

      Pamene ankakomoka mʼmabwalo a mzinda ngati munthu amene wavulazidwa,

      Ndiponso pamene moyo wawo unkachoka ali mʼmanja mwa mayi awo.

  • Zefaniya 1:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Chuma chawo chidzatengedwa ndipo nyumba zawo zidzawonongedwa.+

      Iwo adzamanga nyumba, koma sadzakhalamo.

      Iwo adzalima minda ya mpesa koma sadzamwa vinyo wake.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena