Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Mafumu 20:8-11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Hezekiya anali atafunsa Yesaya kuti: “Kodi chizindikiro+ chakuti Yehova andichiritsa ndipo ndidzapitadi kunyumba ya Yehova pa tsiku lachitatu nʼchiyani?” 9 Yesaya anayankha kuti: “Chizindikiro chochokera kwa Yehova chosonyeza kuti Yehova adzakwaniritsadi mawu ake, ndi ichi: Kodi ukufuna kuti mthunzi uyende masitepe* 10 kupita kutsogolo, kapena uyende masitepe 10 kubwerera mʼmbuyo?”+ 10 Hezekiya anayankha kuti: “Nʼzosavuta kuti mthunzi upite kutsogolo masitepe 10, koma nʼzovuta kuti ubwerere mʼmbuyo masitepe 10.” 11 Choncho mneneri Yesaya anafuulira Yehova ndipo iye anachititsa mthunzi umene unali utapita kale kutsogolo kuti ubwerere mʼmbuyo pamasitepe a Ahazi. Mthunziwo unabwerera mʼmbuyo masitepe 10.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena