Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yeremiya 21:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 ‘“Ndatsimikiza kubweretsa tsoka pamzinda uwu, osati zinthu zabwino,”*+ akutero Yehova. “Mzindawu udzaperekedwa mʼmanja mwa mfumu ya Babulo+ ndipo adzauwotcha ndi moto.”+

  • Yeremiya 32:28, 29
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 28 Choncho Yehova wanena kuti, ‘Tsopano ndikupereka mzindawu mʼmanja mwa Akasidi ndi mʼmanja mwa Nebukadinezara* mfumu ya Babulo, ndipo aulanda.+ 29 Akasidi amene akumenyana ndi anthu amumzindawu adzabwera nʼkuyatsa mzindawu moti udzapseratu.+ Adzawotchanso nyumba zimene pamadenga ake anthu ankaperekerapo nsembe kwa Baala komanso nsembe zachakumwa kwa milungu ina kuti andikhumudwitse.’+

  • Yeremiya 39:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Kenako Akasidi anawotcha nyumba ya mfumu ndi nyumba za anthu+ ndipo anagwetsa mpanda wa Yerusalemu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena