Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yeremiya 11:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Chifukwa milungu yako, iwe Yuda, yafanana ndi mizinda yako kuchuluka kwake. Ndipo chinthu chochititsa manyazi mwachimangira* maguwa ansembe ochuluka mofanana ndi misewu ya mu Yerusalemu, maguwa ansembe oti muziperekerapo nsembe kwa Baala.’+

  • Ezekieli 16:24, 25
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 ‘Unamanga malo oti uzilambirirapo milungu yabodza ndipo unakonza malo okwera mʼbwalo lililonse la mzinda. 25 Unamanga malo ako okwerawo pamalo oonekera bwino kwambiri mumsewu uliwonse ndipo kukongola kwako unakusandutsa chinthu chonyansa podzipereka kwa munthu* aliyense wodutsa+ ndipo unachulukitsa zochita zako zauhulezo.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena