Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yeremiya 32:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Kenako ndinapereka makalata a pangano ogulira mundawo kwa Baruki+ mwana wa Neriya,+ mwana wa Maseya. Ndinapereka makalatawo pamaso pa Hanameli mwana wa mʼbale wawo wa bambo anga, pamaso pa mboni zimene zinasaina makalatawo ndi pamaso pa Ayuda onse amene anali mʼBwalo la Alonda.+

  • Yeremiya 43:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Koma Baruki+ mwana wa Neriya ndi amene akukulimbikitsa kuti unene zinthu zofuna kutipweteketsa nʼcholinga choti mutipereke mʼmanja mwa Akasidi kuti atiphe kapena atitenge kupita ku ukapolo ku Babulo.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena