Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Mafumu 23:36
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 36 Yehoyakimu+ anayamba kulamulira ali ndi zaka 25 ndipo analamulira zaka 11 ku Yerusalemu.+ Mayi ake anali a ku Ruma ndipo dzina lawo linali Zebida mwana wa Pedaya.

  • Yeremiya 25:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 25 Awa ndi mawu amene Yeremiya anauzidwa onena za anthu onse a mu Yuda mʼchaka cha 4 cha ulamuliro wa Yehoyakimu+ mwana wa Yosiya, mfumu ya Yuda, chimenenso chinali chaka choyamba cha ulamuliro wa Nebukadinezara* mfumu ya Babulo.

  • Yeremiya 36:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 36 Ndiyeno mʼchaka cha 4 cha ulamuliro wa Yehoyakimu+ mwana wa Yosiya, mfumu ya Yuda, Yehova anauza Yeremiya kuti:

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena