Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yesaya 41:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Chifukwa ine, Yehova Mulungu wako, ndagwira dzanja lako lamanja,

      Ine amene ndikukuuza kuti, ‘Usachite mantha. Ineyo ndikuthandiza.’+

  • Yesaya 43:1, 2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 43 Tsopano izi ndi zimene Yehova wanena,

      Mlengi wako iwe Yakobo, amene anakupanga iwe Isiraeli.+ Iye wanena kuti:

      “Usachite mantha, chifukwa ine ndakuwombola.+

      Ndakuitana pokutchula dzina lako.

      Iwe ndiwe wanga.

       2 Ukamadzadutsa pamadzi, ine ndidzakhala nawe.+

      Ukamadzawoloka mitsinje, madzi sadzakukokolola.+

      Ukamadzayenda pamoto sudzapsa

      Ndipo ngakhale lawi la moto silidzakuwaula.

  • Yesaya 44:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Yehova, amene anakupanga+

      Ndiponso amene anakuumba,

      Amene wakhala akukuthandiza kuyambira uli mʼmimba,* wanena kuti:

      ‘Usachite mantha, iwe mtumiki wanga Yakobo,+

      Ndiponso iwe Yesuruni,*+ amene ndakusankha.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena