Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yeremiya 25:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Choncho ndinatenga kapu imene inali mʼdzanja la Yehova ndipo ndinamwetsa mitundu yonse imene Yehova ananditumizako. Mitunduyo ndi iyi:+

  • Yeremiya 25:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 ndiponso anthu a mitundu yosiyanasiyana. Mafumu onse amʼdziko la Uzi, mafumu onse amʼdziko la Afilisiti,+ Asikeloni,+ Gaza, Ekironi komanso amene anatsala ku Asidodi,

  • Amosi 1:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 Ndidzapha anthu a ku Asidodi,+

      Komanso wolamulira* wa ku Asikeloni.+

      Ndidzalanga Ekironi,+

      Ndipo ndidzafafaniza Afilisiti otsala,”+ watero Yehova, Ambuye Wamkulu Koposa.’

  • Zefaniya 2:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  5 “Tsoka kwa anthu okhala mʼmbali mwa nyanja, mtundu wa Akereti.+

      Yehova wakudzudzulani.

      Iwe Kanani, dziko la Afilisiti, ndidzakuwononga,

      Moti mʼdziko lako simudzatsala munthu aliyense.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena