Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 19:36, 37
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 36 Choncho ana a Loti awiri onsewo anakhala oyembekezera atagona ndi bambo awo. 37 Mwana woyamba anabereka mwana wamwamuna nʼkumupatsa dzina lakuti Mowabu.+ Iye ndi tate wa Amowabu amasiku ano.+

  • Yesaya 15:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Uwu ndi uthenga wokhudza Mowabu:+

      Chifukwa chakuti wawonongedwa usiku umodzi wokha,

      Ari+ wa ku Mowabu wakhalitsidwa chete.

      Chifukwa chakuti wawonongedwa usiku umodzi wokha,

      Kiri+ wa ku Mowabu wakhalitsidwa chete.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena