Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yeremiya 51:41
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 41 “Taonani! Sesaki* walandidwa,+

      Dziko limene anthu amalitamanda padziko lonse lapansi latengedwa.+

      Babulo wakhala chinthu chochititsa mantha pakati pa mitundu ya anthu.

  • Chivumbulutso 18:15, 16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Amalonda amene ankagulitsa zinthu zimenezi, amene analemera chifukwa cha iye, adzaima patali chifukwa cha mantha poona mmene akuzunzikira ndipo adzamulirira ndi kumva chisoni. 16 Iwo azidzati: ‘Zomvetsa chisoni! Zomvetsa chisoni! Iwe mzinda waukulu, umene unkavala zovala zapamwamba, zapepo ndi zofiira kwambiri. Iwe mzinda umene unakongoletsedwa mochititsa chidwi ndi zodzikongoletsera zagolide, mwala wamtengo wapatali ndi ngale.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena