3 Tsiku limene Yehova adzakupatseni mpumulo ku ululu wanu nʼkuthetsa chipwirikiti komanso ukapolo wanu wowawa,+ 4 mudzanena mwambi uwu wonyoza mfumu ya Babulo:
“Amene ankagwiritsa ntchito anzake mokakamiza uja wawonongedwa!
Kuponderezedwa kuja kwatha ndithu!+