Yeremiya 25:12 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 12 ‘Ndiyeno zaka 70 zimenezo zikadzakwana,+ ndidzalanga mfumu ya Babulo ndi mtundu umenewo chifukwa cha zolakwa zawo.+ Ndipo dziko la Akasidi ndidzalisandutsa bwinja mpaka kalekale,’ akutero Yehova.+ Yeremiya 51:43 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 43 Mizinda yake yakhala chinthu chochititsa mantha, dziko lopanda madzi komanso chipululu. Mizindayo yakhala dziko limene simudzakhalanso munthu aliyense ndipo palibe munthu amene adzadutsemo.+ Yeremiya 51:64 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 64 Ndiyeno ukanene kuti, ‘Umu ndi mmene Babulo adzamirire ndipo sadzatulukanso+ chifukwa cha tsoka limene ndikumugwetsera. Ndipo anthu amene akukhala mumzindawo adzatopa.’”+ Mawu a Yeremiya athera pamenepa.
12 ‘Ndiyeno zaka 70 zimenezo zikadzakwana,+ ndidzalanga mfumu ya Babulo ndi mtundu umenewo chifukwa cha zolakwa zawo.+ Ndipo dziko la Akasidi ndidzalisandutsa bwinja mpaka kalekale,’ akutero Yehova.+
43 Mizinda yake yakhala chinthu chochititsa mantha, dziko lopanda madzi komanso chipululu. Mizindayo yakhala dziko limene simudzakhalanso munthu aliyense ndipo palibe munthu amene adzadutsemo.+
64 Ndiyeno ukanene kuti, ‘Umu ndi mmene Babulo adzamirire ndipo sadzatulukanso+ chifukwa cha tsoka limene ndikumugwetsera. Ndipo anthu amene akukhala mumzindawo adzatopa.’”+ Mawu a Yeremiya athera pamenepa.