Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yeremiya 49:19-21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 “Taona! Wina adzabwera ngati mkango+ kuchokera munkhalango zowirira zamʼmphepete mwa Yorodano. Adzabwera kudzaukira malo otetezeka odyetserako ziweto, koma mʼkanthawi kochepa ndidzamuthamangitsa pamalowo. Ndidzaika pamalopo mtsogoleri amene ndamusankha. Chifukwa ndi ndani amene angafanane ndi ine ndipo ndi ndani angatsutsane nane? Kodi pali mʼbusa amene angakane kuchita zimene ine ndikufuna?+ 20 Tsopano amuna inu, tamverani zimene Yehova wasankha* kuchitira Edomu ndiponso zimene waganiza kuti achitire anthu amene akukhala ku Temani:+

      Ndithudi, chilombo chidzakokera kutali ana a nkhosa.

      Adzachititsa kuti malo awo okhala asanduke bwinja chifukwa cha zimene anthuwo anachita.+

      21 Dziko lapansi lagwedezeka chifukwa cha mkokomo wa kugwa kwawo.

      Kukumveka kulira!

      Kulirako kwamveka mpaka ku Nyanja Yofiira.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena