Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yeremiya 25:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 ‘Ndiyeno zaka 70 zimenezo zikadzakwana,+ ndidzalanga mfumu ya Babulo ndi mtundu umenewo chifukwa cha zolakwa zawo.+ Ndipo dziko la Akasidi ndidzalisandutsa bwinja mpaka kalekale,’ akutero Yehova.+

  • Yeremiya 25:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Chifukwa mitundu yambiri ndi mafumu otchuka+ adzawagwiritsa ntchito ngati akapolo+ ndipo ndidzawabwezera mogwirizana ndi zochita zawo komanso ntchito ya manja awo.’”+

  • Yeremiya 50:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Mufuulireni mfuu yankhondo kuchokera kumbali zonse.

      Iye wavomereza kuti wagonja.*

      Zipilala zake zagwa, mipanda yake yagwetsedwa,+

      Chifukwa Yehova akumubwezera.+

      Inunso mubwezereni.

      Muchitireni zimene iye anakuchitirani.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena