Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Mbiri 28:20-22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Patapita nthawi, Tigilati-pilenesere+ mfumu ya Asuri anabwera kwa iye ndipo anangomuwonjezera mavuto+ mʼmalo momulimbikitsa. 21 Ahazi anali atatenga zinthu za mʼnyumba ya Yehova, za mʼnyumba ya mfumu+ ndi zamʼnyumba za akalonga nʼkuzipereka ngati mphatso kwa mfumu ya Asuri, koma zimenezi sizinamuthandize. 22 Ndipo pa nthawi imene Mfumu Ahazi ankakumana ndi mavuto, anawonjezera kuchita zosakhulupirika kwa Yehova.

  • Yeremiya 2:30
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 30 Ndalanga ana anu aamuna koma sizinathandize.+

      Iwo sanalole kulandira chilango.*+

      Lupanga lanu linapha aneneri anu,+

      Ngati mkango wolusa.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena