Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yesaya 2:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Milungu yopanda phindu idzatheratu.+

  • Yeremiya 51:17, 18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Munthu aliyense akuchita zinthu mopanda nzeru komanso mosazindikira.

      Mmisiri wa zitsulo aliyense adzachita manyazi chifukwa cha chifaniziro chake chosula.+

      Chifukwa chifaniziro chake chopangidwa ndi chitsulo chosungunula ndi mulungu wonama

      Ndipo mafano amenewa alibe mzimu.*+

      18 Iwo ndi achabechabe,+ oyenera kunyozedwa.

      Tsiku loti aweruzidwe likadzafika adzawonongedwa.

  • Zefaniya 2:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Yehova adzawachititsa mantha,

      Chifukwa adzawononga milungu yonse yapadziko lapansi.

      Ndipo zilumba zonse za anthu a mitundu ina zidzamugwadira,*+

      Chilichonse pamalo ake.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena