Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yeremiya 15:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Inu Yehova mukudziwa bwino mavuto anga.

      Ndikumbukireni ndi kundiyangʼana.

      Mundibwezerere anthu amene akundizunza.+

      Musalole kuti ndiwonongeke chifukwa chakuti mukuwalezera mtima.

      Dziwani kuti ndikunyozedwa chifukwa cha inu.+

  • Yeremiya 20:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Koma Yehova anali nane ngati msilikali woopsa.+

      Nʼchifukwa chake anthu amene akundizunza adzakhumudwa ndipo sadzapambana.+

      Adzachita manyazi kwambiri chifukwa zinthu sizidzawayendera bwino.

      Manyazi awo adzakhala nawo mpaka kalekale ndipo sadzaiwalika.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena