Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Mafumu 9:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Nyumbayi idzakhala bwinja.+ Aliyense wodutsa pafupi adzayangʼana modabwa ndipo adzaimba mluzu nʼkunena kuti, ‘Nʼchifukwa chiyani Yehova anachitira zimenezi dzikoli komanso nyumbayi?’+

  • Yeremiya 18:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Choncho dziko lawo lidzakhala chinthu chochititsa mantha+

      Komanso chimene anthu azidzachiimbira mluzu mpaka kalekale.+

      Aliyense wodutsa pafupi ndi dzikoli adzaliyangʼanitsitsa mwamantha ndipo adzapukusa mutu wake.+

  • Maliro 2:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Anthu onse odutsa mumsewu akakuona, akuwomba mʼmanja monyoza.+

      Akuimba mluzu modabwa+ ndipo akupukusira mitu yawo mwana wamkazi wa Yerusalemu. Iwo akunena kuti:

      “Kodi uwu ndi mzinda umene ankaunena kuti, ‘Ndi wokongola kwambiri ndipo anthu padziko lonse lapansi amasangalala nawoʼ?”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena