Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yeremiya 8:1, 2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 “Pa nthawi imeneyo,” akutero Yehova, “mafupa a mafumu a Yuda, a akalonga awo, a ansembe, a aneneri ndi a anthu okhala mu Yerusalemu adzatulutsidwa mʼmanda awo. 2 Mafupawo adzamwazidwa padzuwa, pamwezi ndi panyenyezi zonse zakumwamba* zimene ankazikonda, kuzitumikira, kuzitsatira, kuzifunafuna ndi kuzigwadira.+ Anthu sadzasonkhanitsa mafupawo pamodzi nʼkuwaika mʼmanda ndipo adzakhala ngati manyowa panthaka.”+

  • Zefaniya 1:4, 5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 “Ndidzatambasula dzanja langa nʼkuwononga Yuda,

      Ndiponso anthu onse okhala mu Yerusalemu.

      Ndidzawononga chilichonse chokhudza Baala+ pamalowa.

      Ndidzawononganso ansembe komanso dzina la ansembe a mulungu wachilendo.+

       5 Ndidzawononga anthu amene amakwera padenga nʼkumagwadira magulu a zinthu zakumwamba.*+

      Komanso amene amagwada ndiponso kulumbira kuti adzakhala okhulupirika kwa Yehova+

      Koma nʼkumalumbiranso kuti adzakhala okhulupirika kwa Malikamu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena