Deuteronomo 33:28 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 28 Isiraeli adzakhala motetezeka,Kasupe wa Yakobo adzakhala motetezeka,Mʼdziko lokhala ndi chakudya komanso vinyo watsopano,+Limene kumwamba kwake kudzagwetsa mame.+ Yeremiya 32:37 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 37 ‘Ine ndidzawasonkhanitsa pamodzi kuchokera kumayiko onse kumene ndinawabalalitsira nditakwiya, kupsa mtima ndiponso ndili ndi ukali waukulu.+ Ndidzawabwezeretsa mʼdziko lino nʼkuwachititsa kuti azikhala motetezeka.+ Zekariya 14:11 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 11 Anthu adzakhala mumzindawo ndipo sudzatembereredwanso kuti uwonongedwe.+ Anthu azidzakhala mu Yerusalemu motetezeka.+
28 Isiraeli adzakhala motetezeka,Kasupe wa Yakobo adzakhala motetezeka,Mʼdziko lokhala ndi chakudya komanso vinyo watsopano,+Limene kumwamba kwake kudzagwetsa mame.+
37 ‘Ine ndidzawasonkhanitsa pamodzi kuchokera kumayiko onse kumene ndinawabalalitsira nditakwiya, kupsa mtima ndiponso ndili ndi ukali waukulu.+ Ndidzawabwezeretsa mʼdziko lino nʼkuwachititsa kuti azikhala motetezeka.+
11 Anthu adzakhala mumzindawo ndipo sudzatembereredwanso kuti uwonongedwe.+ Anthu azidzakhala mu Yerusalemu motetezeka.+