Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yeremiya 16:14, 15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 ‘Komabe masiku akubwera,’ akutero Yehova, ‘pamene sadzalumbiranso kuti: “Pali Yehova Mulungu wamoyo amene anatulutsa Aisiraeli mʼdziko la Iguputo!”+ 15 Koma adzalumbira kuti: “Pali Yehova Mulungu wamoyo amene anatulutsa Aisiraeli mʼdziko lakumpoto komanso kuchokera mʼmayiko onse kumene anawabalalitsira!” Ineyo ndidzawabwezera kudziko lawo limene ndinapatsa makolo awo.’+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena