Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Mbiri 33:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 33 Manase+ anayamba kulamulira ali ndi zaka 12 ndipo analamulira zaka 55 ku Yerusalemu.+

  • 2 Mbiri 33:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Iye anamanga maguwa ansembe a gulu lonse la zinthu zakumwamba mʼmabwalo awiri a nyumba ya Yehova.+

  • 2 Mbiri 36:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Anthu ndi atsogoleri onse a ansembe anali osakhulupirika ngakhale pangʼono ndipo ankachita zonyansa zonse zimene anthu a mitundu ina ankachita. Iwo anaipitsa nyumba ya Yehova+ imene iye anaiyeretsa ku Yerusalemu.

  • Yeremiya 7:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Kodi nyumba iyi, imene imatchedwa ndi dzina langa, mwayamba kuiona ngati phanga la achifwamba?+ Inetu ndaona zimene mukuchita,” akutero Yehova.

  • Ezekieli 8:10, 11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Choncho ndinalowa ndipo nditayangʼana ndinaona zithunzi za zinthu zosiyanasiyana zokwawa, nyama zonyansa+ komanso mafano onse onyansa* a Aisiraeli.+ Zithunzizo zinajambulidwa pamakoma onse mochita kugoba. 11 Ndipo akuluakulu 70 a nyumba ya Isiraeli anali ataimirira patsogolo pa mafanowo. Pakati pawo panalinso Yaazaniya mwana wa Safani.+ Aliyense ananyamula chiwaya chofukizira nsembe mʼmanja mwake ndipo utsi wonunkhira wa zofukizazo unkakwera mʼmwamba.+

  • Ezekieli 23:39
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 39 Atapha ana awo aamuna nʼkuwapereka nsembe kwa mafano onyansa,+ tsiku lomwelo anabwera kumalo anga opatulika kudzawadetsa.+ Izi ndi zimene anachita mʼnyumba yanga.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena