-
Ezekieli 13:7Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
7 Kodi masomphenya amene mwaonawa si abodza ndipo zimene mwaloserazi si zonama pamene mukunena kuti, ‘Yehova wanena kuti,’ pamene ine sindinanene chilichonse?”’
-