Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 13:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Koma mneneri kapena woloserayo muzimupha,+ chifukwa akulimbikitsa anthu kuti azipandukira Yehova Mulungu wanu amene anakutulutsani mʼdziko la Iguputo komanso kukuwombolani mʼnyumba yaukapolo. Munthu ameneyo akufuna akupatutseni panjira imene Yehova Mulungu wanu anakulamulani kuti muziyendamo. Choncho muzichotsa woipayo pakati panu.+

  • Deuteronomo 18:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Ngati mneneri wina angadzikuze nʼkulankhula mʼdzina langa mawu amene sindinamulamule kuti alankhule, kapena kulankhula mʼdzina la milungu ina, mneneri ameneyo afe ndithu.+

  • Yeremiya 29:32
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 32 Yehova wanena kuti, ‘Ine ndilanga Semaya wa ku Nehelamu ndi mbadwa zake. Sipadzapezeka mwamuna aliyense wochokera mʼbanja lake amene adzapulumuke pakati pa anthu awa. Ndipo iye sadzaona zabwino zimene ndidzachitire anthu anga chifukwa walimbikitsa anthu kuti apandukire Yehova,’ akutero Yehova.”’”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena