Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yesaya 30:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Iwo amapita ku Iguputo+ asanandifunse,+

      Kuti akapeze chitetezo kwa Farao*

      Ndiponso kuti akabisale mumthunzi wa Iguputo.

  • Yeremiya 44:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Ine ndigwira anthu amene anatsala ku Yuda omwe anatsimikiza mtima kuti apite mʼdziko la Iguputo nʼkumakakhala kumeneko, moti onsewo adzafera mʼdziko la Iguputo.+ Iwo adzaphedwa ndi lupanga komanso adzafa ndi njala. Kuyambira munthu wamba ndi wolemekezeka yemwe, onse adzaphedwa ndi lupanga komanso adzafa ndi njala. Iwo adzakhala otembereredwa, chinthu chochititsa mantha, chinthu chonyozeka ndi chochititsa manyazi.+

  • Ezekieli 17:17, 18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Gulu lalikulu la asilikali komanso asilikali ambirimbiri a Farao sadzamuthandiza pankhondo,+ adani akadzamanga malo okwera omenyerapo nkhondo ndiponso mpanda womenyerapo nkhondo nʼcholinga chakuti aphe anthu ambiri. 18 Iye wanyoza lumbiro limenelo komanso waphwanya pangano. Ngakhale kuti analonjeza,* iye wachita zinthu zonsezi ndipo sadzapulumuka.”’

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena