Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Mbiri 20:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 Aamoni ndi Amowabu anaukira anthu okhala kudera lamapiri la Seiri+ ndipo anayamba kuwapha mpaka kuwamaliza. Atatha kupha anthu a ku Seiri, iwo anaphana okhaokha.+

  • Hagai 2:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Ndidzagonjetsa maufumu ndi kuchotsa mphamvu za maufumu a anthu a mitundu ina.+ Ndidzawononga magaleta* ndi okwera pamagaletawo. Mahatchi* ndi okwera pamahatchiwo adzaphedwa ndipo aliyense adzaphedwa ndi mʼbale wake ndi lupanga.’”+

  • Zekariya 14:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Pa tsiku limenelo Yehova adzawasokoneza kwambiri. Aliyense adzagwira dzanja la mnzake ndipo aliyense adzamenya mnzake.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena