Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ezekieli 8:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Kenako iye anatambasula chinachake chooneka ngati dzanja ndipo anagwira tsitsi lakumutu kwanga nʼkundinyamula. Ndiyeno mzimu unandinyamulira mʼmalere pakati pa dziko lapansi ndi kumwamba, nʼkundipititsa ku Yerusalemu mʼmasomphenya ochokera kwa Mulungu. Mzimuwo unandifikitsa pakhomo la geti la bwalo lamkati+ loyangʼana kumpoto pamene panali fano loimira nsanje, limene limachititsa nsanje.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena