Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ezekieli 40:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Kumbali iliyonse ya geti lakumʼmawa kunali zipinda zitatu za alonda. Zipinda zitatuzo zinali zazikulu mofanana, ndipo zipilala zamʼmbali zimene zinali mbali iliyonse zinalinso zofanana.

  • Ezekieli 43:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 43 Kenako munthu uja anandipititsa kugeti limene linayangʼana kumʼmawa.+

  • Ezekieli 43:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Ndiyeno ulemerero wa Yehova unalowa mʼkachisi* kudzera pageti limene linayangʼana kumʼmawa.+

  • Ezekieli 46:1, 2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 46 “Yehova, Ambuye Wamkulu Koposa, wanena kuti: ‘Kanyumba kapageti la bwalo lamkati kamene kayangʼana kumʼmawa+ kazikhala kotseka+ kwa masiku 6 ogwira ntchito.+ Koma pa tsiku la Sabata ndi pa tsiku limene mwezi watsopano waoneka kazitsegulidwa. 2 Mtsogoleri azilowa kuchokera panja kudzera pakhonde la kanyumba kapagetiko+ ndipo aziima pafupi ndi felemu lagetilo. Ndiyeno ansembe azimuperekera nsembe yopsereza yathunthu ndi nsembe zake zamgwirizano. Mtsogoleriyo azigwada nʼkuwerama pakhomo la kanyumba kapageti kenako nʼkutuluka. Koma getilo lisamatsekedwe mpaka madzulo.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena