Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Levitiko 1:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Ngati akupereka ngʼombe kuti ikhale nsembe yake yopsereza, azipereka yamphongo, yopanda chilema.+ Aziipereka kwa Yehova mwa kufuna kwake,+ pakhomo la chihema chokumanako.

  • Levitiko 1:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Nyama ya nsembe yopserezayo aziisenda nʼkuiduladula.+

  • Levitiko 8:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Anaduladula nkhosayo ndipo Mose anatenga mutu wake, nyama yoduladulayo ndi mafuta ake,* nʼkuziwotcha.

  • Ezekieli 43:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Ndiyeno munthu uja anandiuza kuti, “Iwe mwana wa munthu, Yehova, Ambuye Wamkulu Koposa wanena kuti: ‘Amenewa ndi malangizo amene akuyenera kutsatiridwa popanga guwa lansembe kuti aziperekerapo nsembe zopsereza zathunthu ndi kuwazapo magazi.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena