Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Mafumu 22:21, 22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Kenako mngelo*+ wina anabwera kudzaima pamaso pa Yehova nʼkunena kuti, ‘Ine ndikamʼpusitsa.’ Yehova anamufunsa kuti, ‘Ukamʼpusitsa bwanji?’ 22 Iye anayankha kuti, ‘Ndipita kukakhala mzimu wabodza mʼkamwa mwa aneneri ake onse.’+ Ndiyeno Mulungu anati, ‘Ukamʼpusitsadi ndipo zikakuyendera bwino. Pita ukachite zimenezo.’

  • Yeremiya 4:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Kenako ndinanena kuti: “Mayo ine Yehova, Ambuye Wamkulu Koposa! Kunena zoona, mwapusitsa kwambiri anthu awa+ ndiponso Yerusalemu ponena kuti, ‘Mudzakhala pa mtendere,’+ pamene lupanga lili pakhosi pathu.”*

  • 2 Atesalonika 2:10, 11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 komanso akugwiritsa ntchito njira iliyonse yachinyengo+ kuti apusitse amene akupita kukawonongedwa. Izi zidzakhala chilango kwa iwo chifukwa sanalandire komanso kukonda choonadi kuti adzapulumuke. 11 Nʼchifukwa chake Mulungu walola kuti iwo apusitsidwe ndi ziphunzitso zabodza nʼcholinga choti azikhulupirira bodza,+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena