Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Oweruza 2:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Koma woweruza akamwalira, iwo ankayambiranso kuchita zoipa kuposa makolo awo. Ankatsatira milungu ina, kuitumikira ndi kuigwadira.+ Iwo sanasiye zochita zawozo ndiponso unkhutukumve wawo.

  • 2 Mbiri 21:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Koma wayenda mʼnjira ya mafumu a Isiraeli+ nʼkuchititsa kuti Yuda ndi anthu a ku Yerusalemu achite uhule wauzimu+ ngati uhule wa anthu a mʼbanja la Ahabu.+ Waphanso ngakhale azichimwene ako,+ anthu a mʼnyumba ya bambo ako, amene anali abwino kuposa iweyo.

  • Yeremiya 13:26, 27
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 26 Choncho ndidzakuvula siketi yako nʼkukuphimba nayo kumaso,

      Ndipo anthu adzaona maliseche ako.+

      27 Chigololo chimene ukuchita,+ kumemesa* kwako,

      Khalidwe lako lonyansa* la uhule, zonsezi zidzaonekera.

      Ndaona khalidwe lako lonyansa+

      Mʼmapiri komanso kuthengo.

      Tsoka kwa iwe Yerusalemu!

      Kodi ukhalabe wodetsedwa mpaka liti?”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena