Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 32:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Mkwiyo wanga wayatsa moto+

      Umene udzayaka mpaka kukafika pansi penipeni pa Manda,*+

      Ndipo udzapsereza dziko lapansi ndi zokolola zake,

      Komanso udzayatsa maziko a mapiri.

  • Yeremiya 21:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Ndidzakupatsani chilango

      Mogwirizana ndi zochita zanu,’+ akutero Yehova.

      ‘Ndipo ndidzayatsa moto munkhalango za mzindawu,

      Moti udzapsereza zinthu zonse zimene zili pafupi ndi mzindawu.’”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena