Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yeremiya 49:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 49 Ponena za Aamoni+ Yehova wanena kuti:

      “Kodi Isiraeli alibe ana aamuna?

      Kodi alibe wolandira cholowa?

      Nʼchifukwa chiyani Malikamu+ watenga Gadi+ kuti akhale cholowa chake?

      Ndipo nʼchifukwa chiyani anthu ake akukhala mʼmizinda ya Isiraeli?”

  • Amosi 1:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Yehova wanena kuti,

      ‘“Chifukwa chakuti Aamoni andigalukira mobwerezabwereza,+ sindidzawasinthira chigamulo changa.

      Chifukwa anatumbula akazi apakati a ku Giliyadi kuti akulitse malo awo okhala.+

  • Zefaniya 2:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  9 Yehova wa magulu ankhondo akumwamba, Mulungu wa Isiraeli wanena kuti: “Pali ine Mulungu wamoyo,

      Mowabu adzakhala ngati Sodomu,+

      Ndipo Amoni adzakhala ngati Gomora,+

      Malo okhala ndi zomera zoyabwa, dothi lamchere ndiponso malo abwinja mpaka kalekale.+

      Anthu anga amene adzatsale adzatenga zinthu za anthu amenewa,

      Ndipo anthu amtundu wanga amene adzatsale, adzawalanda anthuwa zinthu zawo.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena