Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yoweli 3:4-6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Komanso kodi ndakulakwira chiyani

      Iwe Turo ndi Sidoni ndiponso nonse amʼchigawo cha Filisitiya?

      Kodi mukundichitira zimenezi pondibwezera zimene ndinachita?

      Ngati mukundibwezera,

      Ine ndidzakubwezerani mwamsanga ndiponso mofulumira zimene mwandichitirazo.+

       5 Chifukwa chakuti mwatenga siliva ndi golide wanga,+

      Ndipo mwabweretsa zinthu zanga zabwino kwambiri mu akachisi anu,

       6 Komanso mwagulitsa anthu a ku Yuda ndi a ku Yerusalemu kwa Agiriki,+

      Kuti muwapititse kutali ndi dziko lawo,

  • Amosi 1:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  9 Yehova wanena kuti,

      ‘Popeza Turo anandigalukira mobwerezabwereza,+ sindidzamusinthira chigamulo changa.

      Chifukwa anapereka ku Edomu gulu lonse la anthu ogwidwa ukapolo,

      Ndiponso chifukwa chakuti sanakumbukire pangano la pachibale.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena