Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yesaya 30:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Iwo amapita ku Iguputo+ asanandifunse,+

      Kuti akapeze chitetezo kwa Farao*

      Ndiponso kuti akabisale mumthunzi wa Iguputo.

  • Yesaya 36:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Choncho Rabisake anawauza kuti: “Mukauze Hezekiya kuti, ‘Mfumu yaikulu, mfumu ya Asuri yanena kuti: “Kodi ukudalira chiyani?+

  • Yesaya 36:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Ukudalira thandizo la Iguputo, bango lophwanyika loti munthu ataligwira kuti alitsamire, lingamucheke mʼmanja. Ndi mmene zilili ndi Farao mfumu ya Iguputo kwa onse omudalira.+

  • Yeremiya 2:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Ndiye nʼchifukwa chiyani ukufuna kuyenda mʼnjira ya ku Iguputo+

      Kuti ukamwe madzi amumtsinje wa Sihori?*

      Nʼchifukwa chiyani ukufuna kuyenda mʼnjira yopita kudziko la Asuri+

      Kuti ukamwe madzi amumtsinje wa Firate?

  • Yeremiya 37:5-7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Ndiyeno asilikali a Farao anabwera kuchokera ku Iguputo+ ndipo Akasidi amene anali atazungulira mzinda wa Yerusalemu atamva zimenezi anachoka ku Yerusalemu.+ 6 Kenako Yehova anauza mneneri Yeremiya kuti: 7 “Yehova Mulungu wa Isiraeli wanena kuti, ‘Mfumu ya Yuda imene yakutumani kudzafunsira kwa ine mukaiuze kuti: “Taonani! Asilikali a Farao amene akubwera kudzakuthandizani adzabwerera kwawo ku Iguputo.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena